×

Kumwamba kumafuna kuphulika chifukwa cha ulemerero wake ndipo angelo amaimba mayamiko a 42:5 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Ash-Shura ⮕ (42:5) ayat 5 in Chichewa

42:5 Surah Ash-Shura ayat 5 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Ash-Shura ayat 5 - الشُّوري - Page - Juz 25

﴿تَكَادُ ٱلسَّمَٰوَٰتُ يَتَفَطَّرۡنَ مِن فَوۡقِهِنَّۚ وَٱلۡمَلَٰٓئِكَةُ يُسَبِّحُونَ بِحَمۡدِ رَبِّهِمۡ وَيَسۡتَغۡفِرُونَ لِمَن فِي ٱلۡأَرۡضِۗ أَلَآ إِنَّ ٱللَّهَ هُوَ ٱلۡغَفُورُ ٱلرَّحِيمُ ﴾
[الشُّوري: 5]

Kumwamba kumafuna kuphulika chifukwa cha ulemerero wake ndipo angelo amaimba mayamiko a Ambuye wawo ndipo amapempha chikhululukiro cha zolengedwa zonse za padziko lapansi. Ndithudi, Mulungu, ndiye amene amakhululukira ndipo ndi Mwini chisoni chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: تكاد السموات يتفطرن من فوقهن والملائكة يسبحون بحمد ربهم ويستغفرون لمن في, باللغة نيانجا

﴿تكاد السموات يتفطرن من فوقهن والملائكة يسبحون بحمد ربهم ويستغفرون لمن في﴾ [الشُّوري: 5]

Khaled Ibrahim Betala
“(Chifukwa chakukula Kwake ndi ulemelero Wake) mitambo ikuyandikira kuphwasuka pamwamba pa iyo. Ndipo angelo akulemekeza ndi kutamanda Mbuye wawo, ndi kuwapemphera chikhululuko amene ali pa dziko lapansi. Dziwani kuti ndithu Allah Yekha ndiye Wokhululuka kwabasi, Wachisoni chosatha
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek