×

Ndipo Farawo adalengeza pamaso pa anthu ake kuti, “Oh inu anthu anga! 43:51 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Az-Zukhruf ⮕ (43:51) ayat 51 in Chichewa

43:51 Surah Az-Zukhruf ayat 51 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Az-Zukhruf ayat 51 - الزُّخرُف - Page - Juz 25

﴿وَنَادَىٰ فِرۡعَوۡنُ فِي قَوۡمِهِۦ قَالَ يَٰقَوۡمِ أَلَيۡسَ لِي مُلۡكُ مِصۡرَ وَهَٰذِهِ ٱلۡأَنۡهَٰرُ تَجۡرِي مِن تَحۡتِيٓۚ أَفَلَا تُبۡصِرُونَ ﴾
[الزُّخرُف: 51]

Ndipo Farawo adalengeza pamaso pa anthu ake kuti, “Oh inu anthu anga! Kodi Ufumu wa dziko la Aiguputo si wanga? Nanga mitsinje imene ilikuyenda pansi pa mapazi anga, kodi simuli kuiona?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ونادى فرعون في قومه قال ياقوم أليس لي ملك مصر وهذه الأنهار, باللغة نيانجا

﴿ونادى فرعون في قومه قال ياقوم أليس لي ملك مصر وهذه الأنهار﴾ [الزُّخرُف: 51]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Farawo adaitana anthu ake, adati: “E inu anthu anga! Kodi ulamuliro wa mu Iguputo siwanga pamodzi ndi mitsinje iyi imene ikuyenda pansi panga (pa nyumba zanga?) Kodi simukuona?”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek