×

Motero pirira monga momwe Atumwi akale opirira anali kuchitira ndipo usafune kuti 46:35 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:35) ayat 35 in Chichewa

46:35 Surah Al-Ahqaf ayat 35 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 35 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿فَٱصۡبِرۡ كَمَا صَبَرَ أُوْلُواْ ٱلۡعَزۡمِ مِنَ ٱلرُّسُلِ وَلَا تَسۡتَعۡجِل لَّهُمۡۚ كَأَنَّهُمۡ يَوۡمَ يَرَوۡنَ مَا يُوعَدُونَ لَمۡ يَلۡبَثُوٓاْ إِلَّا سَاعَةٗ مِّن نَّهَارِۭۚ بَلَٰغٞۚ فَهَلۡ يُهۡلَكُ إِلَّا ٱلۡقَوۡمُ ٱلۡفَٰسِقُونَ ﴾
[الأحقَاف: 35]

Motero pirira monga momwe Atumwi akale opirira anali kuchitira ndipo usafune kuti chilango chawo chidze pa iwo mwamsanga. Patsiku limene iwo adzaona zimene ali kulonjezedwa, iwo adzaoneka ngati kuti adangokhala padziko lapansi ola limodzi lokha. Udindo wako ndi kupereka uthenga. Palibe wina amene adzaonongeke kupatula yekhayo amene amaswa malamulo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فاصبر كما صبر أولو العزم من الرسل ولا تستعجل لهم كأنهم يوم, باللغة نيانجا

﴿فاصبر كما صبر أولو العزم من الرسل ولا تستعجل لهم كأنهم يوم﴾ [الأحقَاف: 35]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho pirira (Mtumiki {s.a.w}) monga adapirira aneneri, eni mphamvu ndi kulimba pa chipembedzo, (monga Nuh. Ibrahimu, Mûsa ndi Isa (Yesu); ndipo usawachitire changu. Tsiku limene adzaziona zimene adalonjezedwa kudzakhala monga iwo sadakhalitse pa dziko koma ngati adakhala ola limodzi lokha lamasana. (Zomwe mukuuzidwazi) ndi ulaliki okwana. Palibe adzaonongedwe (ndi chilango cha Allah), kupatula anthu ochimwa (otuluka m’chilamulo cha Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek