×

Ndipo patsiku limene onse osakhulupirira adzaonetsedwa moto, iwo adzafunsidwa kuti, “Kodi ichi 46:34 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:34) ayat 34 in Chichewa

46:34 Surah Al-Ahqaf ayat 34 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 34 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿وَيَوۡمَ يُعۡرَضُ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ عَلَى ٱلنَّارِ أَلَيۡسَ هَٰذَا بِٱلۡحَقِّۖ قَالُواْ بَلَىٰ وَرَبِّنَاۚ قَالَ فَذُوقُواْ ٱلۡعَذَابَ بِمَا كُنتُمۡ تَكۡفُرُونَ ﴾
[الأحقَاف: 34]

Ndipo patsiku limene onse osakhulupirira adzaonetsedwa moto, iwo adzafunsidwa kuti, “Kodi ichi si choonadi?” Iwo adzati, “Inde pali Ambuye wathu!” Ndipo Iye adzati, “Tsopano lawani chilango chimene inu munali kunena kuti ndi bodza.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويوم يعرض الذين كفروا على النار أليس هذا بالحق قالوا بلى وربنا, باللغة نيانجا

﴿ويوم يعرض الذين كفروا على النار أليس هذا بالحق قالوا بلى وربنا﴾ [الأحقَاف: 34]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (akumbutse za) tsiku limene adzaperekedwa ku moto amene sadakhulupirire (uku akuuzidwa): “Kodi izi sizoona?” Adzanena: “Inde, pali Mbuye wathu!” (Allah) adzanena: “Choncho, lawani chilango chifukwa cha kukana kwanu (choonadi).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek