×

Nena, “Kodi mudayamba mwaganiza za zimene mumapembedza zoonjezera pa Mulungu? Ndilangizeni za 46:4 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ahqaf ⮕ (46:4) ayat 4 in Chichewa

46:4 Surah Al-Ahqaf ayat 4 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ahqaf ayat 4 - الأحقَاف - Page - Juz 26

﴿قُلۡ أَرَءَيۡتُم مَّا تَدۡعُونَ مِن دُونِ ٱللَّهِ أَرُونِي مَاذَا خَلَقُواْ مِنَ ٱلۡأَرۡضِ أَمۡ لَهُمۡ شِرۡكٞ فِي ٱلسَّمَٰوَٰتِۖ ٱئۡتُونِي بِكِتَٰبٖ مِّن قَبۡلِ هَٰذَآ أَوۡ أَثَٰرَةٖ مِّنۡ عِلۡمٍ إِن كُنتُمۡ صَٰدِقِينَ ﴾
[الأحقَاف: 4]

Nena, “Kodi mudayamba mwaganiza za zimene mumapembedza zoonjezera pa Mulungu? Ndilangizeni za zimene zidalenga padziko lapansi? Kapena kodi izo zili ndi gawo m’zinthu zimene zili kumwamba? Bweretsani kwa ine Buku limene lidalipo ili lisanadze kapena nzeru zina zotsatira ngati inu muli kunena zoonadi.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل أرأيتم ما تدعون من دون الله أروني ماذا خلقوا من الأرض, باللغة نيانجا

﴿قل أرأيتم ما تدعون من دون الله أروني ماذا خلقوا من الأرض﴾ [الأحقَاف: 4]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: Tandiuzani amene mukuwapembedza ndi kumusiya Allah, ndisonyezeni chimene adalenga panthaka? Kapena ali ndi gawo la kuthangata polenga thambo? Ndibweretsereni buku limene lidadza kale, ili lisanadze, kapena zizindikiro zanzeru, ngati inu mukunena zoona
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek