×

Taonani! Inu ndinu amene mwaitanidwa kupereka m’njira ya Mulungu koma pakati panu 47:38 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Muhammad ⮕ (47:38) ayat 38 in Chichewa

47:38 Surah Muhammad ayat 38 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Muhammad ayat 38 - مُحمد - Page - Juz 26

﴿هَٰٓأَنتُمۡ هَٰٓؤُلَآءِ تُدۡعَوۡنَ لِتُنفِقُواْ فِي سَبِيلِ ٱللَّهِ فَمِنكُم مَّن يَبۡخَلُۖ وَمَن يَبۡخَلۡ فَإِنَّمَا يَبۡخَلُ عَن نَّفۡسِهِۦۚ وَٱللَّهُ ٱلۡغَنِيُّ وَأَنتُمُ ٱلۡفُقَرَآءُۚ وَإِن تَتَوَلَّوۡاْ يَسۡتَبۡدِلۡ قَوۡمًا غَيۡرَكُمۡ ثُمَّ لَا يَكُونُوٓاْ أَمۡثَٰلَكُم ﴾
[مُحمد: 38]

Taonani! Inu ndinu amene mwaitanidwa kupereka m’njira ya Mulungu koma pakati panu pali anthu omwe ndi mbombo. Ndipo aliyense amene achita umbombo amadzimana yekha. Mulungu sasowa kanthu pamene inu ndinu osauka. Ndipo ngati inu mubwerera m’mbuyo Iye adzaika m’malo mwanu anthu ena ndipo sadzakhala olingana ndi inu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: هاأنتم هؤلاء تدعون لتنفقوا في سبيل الله فمنكم من يبخل ومن يبخل, باللغة نيانجا

﴿هاأنتم هؤلاء تدعون لتنفقوا في سبيل الله فمنكم من يبخل ومن يبخل﴾ [مُحمد: 38]

Khaled Ibrahim Betala
“Ha! Ndinu amene mukuitanidwa kuti mupereke (chuma) mu njira ya Allah. Koma alipo ena a inu akuumira ndipo amene akuumira akuzimana yekha. Allah Ngwachikwanekwane ndipo inu ndinu amphawi. Ngati munyoza (Chisilamu) ndi kubwerera m’mbuyo posakhulupirira) Allah adzabweretsa m’malo mwanu anthu ena; iwo sadzakhala ngati inu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek