×

Ndipo akhoza kulanga anthu a chinyengo, aamuna ndi aakazi ndi anthu opembedza 48:6 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Fath ⮕ (48:6) ayat 6 in Chichewa

48:6 Surah Al-Fath ayat 6 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Fath ayat 6 - الفَتح - Page - Juz 26

﴿وَيُعَذِّبَ ٱلۡمُنَٰفِقِينَ وَٱلۡمُنَٰفِقَٰتِ وَٱلۡمُشۡرِكِينَ وَٱلۡمُشۡرِكَٰتِ ٱلظَّآنِّينَ بِٱللَّهِ ظَنَّ ٱلسَّوۡءِۚ عَلَيۡهِمۡ دَآئِرَةُ ٱلسَّوۡءِۖ وَغَضِبَ ٱللَّهُ عَلَيۡهِمۡ وَلَعَنَهُمۡ وَأَعَدَّ لَهُمۡ جَهَنَّمَۖ وَسَآءَتۡ مَصِيرٗا ﴾
[الفَتح: 6]

Ndipo akhoza kulanga anthu a chinyengo, aamuna ndi aakazi ndi anthu opembedza mafano, amuna ndi akazi amene amaganiza zoipa za Mulungu. Kwa iwo kudzadza mavuto ndipo mkwiyo wa Mulungu uli pa iwo. Iye wawatemberera iwo ndipo wakonzekera Gahena omwe ndi malo oipa kukhalako

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويعذب المنافقين والمنافقات والمشركين والمشركات الظانين بالله ظن السوء عليهم دائرة السوء, باللغة نيانجا

﴿ويعذب المنافقين والمنافقات والمشركين والمشركات الظانين بالله ظن السوء عليهم دائرة السوء﴾ [الفَتح: 6]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndi kuti awalange achiphamaso aamuna ndi aakazi ndi omphatikiza Allah aamuna ndi aakazi oganizira Allah maganizo achabe. Kutembenuka koipa kuli kwa iwo ndipo Allah wawakwiyira ndiponso wawatembelera ndi kuwakonzera Jahannamu. Ndipo kumeneko nkobwerera koipa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek