×

Ndi cholinga chakuti inu anthu mukhoza kukhulupirira mwa Mulungu ndi Mtumwi wake 48:9 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Fath ⮕ (48:9) ayat 9 in Chichewa

48:9 Surah Al-Fath ayat 9 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Fath ayat 9 - الفَتح - Page - Juz 26

﴿لِّتُؤۡمِنُواْ بِٱللَّهِ وَرَسُولِهِۦ وَتُعَزِّرُوهُ وَتُوَقِّرُوهُۚ وَتُسَبِّحُوهُ بُكۡرَةٗ وَأَصِيلًا ﴾
[الفَتح: 9]

Ndi cholinga chakuti inu anthu mukhoza kukhulupirira mwa Mulungu ndi Mtumwi wake ndi kuti mumuthandize ndi kumulemekeza iye ndipo kuti muzilemekeza Mulungu m’mawa ndi madzulo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لتؤمنوا بالله ورسوله وتعزروه وتوقروه وتسبحوه بكرة وأصيلا, باللغة نيانجا

﴿لتؤمنوا بالله ورسوله وتعزروه وتوقروه وتسبحوه بكرة وأصيلا﴾ [الفَتح: 9]

Khaled Ibrahim Betala
“Ncholinga choti mumkhulupirire Allah ndi Mtumiki Wake, ndi kuti mumtukule ndi kumulemekeza (Mtumiki) ndi kutinso mumtamande (Allah) m’mawa ndi madzulo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek