×

Anthu okhala m’midzi amati, “Ife timakhulupirira.” Nena, “Inu mulibe chikhulupiriro. Koma nenani 49:14 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hujurat ⮕ (49:14) ayat 14 in Chichewa

49:14 Surah Al-hujurat ayat 14 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hujurat ayat 14 - الحُجُرَات - Page - Juz 26

﴿۞ قَالَتِ ٱلۡأَعۡرَابُ ءَامَنَّاۖ قُل لَّمۡ تُؤۡمِنُواْ وَلَٰكِن قُولُوٓاْ أَسۡلَمۡنَا وَلَمَّا يَدۡخُلِ ٱلۡإِيمَٰنُ فِي قُلُوبِكُمۡۖ وَإِن تُطِيعُواْ ٱللَّهَ وَرَسُولَهُۥ لَا يَلِتۡكُم مِّنۡ أَعۡمَٰلِكُمۡ شَيۡـًٔاۚ إِنَّ ٱللَّهَ غَفُورٞ رَّحِيمٌ ﴾
[الحُجُرَات: 14]

Anthu okhala m’midzi amati, “Ife timakhulupirira.” Nena, “Inu mulibe chikhulupiriro. Koma nenani kuti, “Tadzipereka kwa Mulungu chifukwa chikhulupiriro sichidakhazikike m’mitima mwanu. Ndipo ngati inu mumvera Mulungu ndi Mtumwi wake, Iye sadzachepetsa ntchito zanu, ngakhale m’pang’ono pomwe. Ndithudi Mulungu ndi wokhululukira nthawi zonse ndi Mwini chisoni chosatha.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالت الأعراب آمنا قل لم تؤمنوا ولكن قولوا أسلمنا ولما يدخل الإيمان, باللغة نيانجا

﴿قالت الأعراب آمنا قل لم تؤمنوا ولكن قولوا أسلمنا ولما يدخل الإيمان﴾ [الحُجُرَات: 14]

Khaled Ibrahim Betala
“Arabu akumidzi adanena (kuti): “Takhulupirira.” Nena, Simudakhulupirire (kwenikweni); koma nenani (kuti): “Tagonjera (Allah).” Ndipo mpaka pano chikhulupiliro sichidalowe m’mitima mwanu (ndi kukhazikika bwinobwino). Koma ngati mumvera Allah ndi Mtumiki Wake, sakuchepetserani chilichonse m’zochita zanu. Ndithu Allah Ngokhululuka kwabasi, Ngwachifundo chambiri
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek