×

Koma ngati zidziwika kuti anthu awiriwa ali ndi mlandu wina, sankhulani anthu 5:107 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:107) ayat 107 in Chichewa

5:107 Surah Al-Ma’idah ayat 107 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 107 - المَائدة - Page - Juz 7

﴿فَإِنۡ عُثِرَ عَلَىٰٓ أَنَّهُمَا ٱسۡتَحَقَّآ إِثۡمٗا فَـَٔاخَرَانِ يَقُومَانِ مَقَامَهُمَا مِنَ ٱلَّذِينَ ٱسۡتَحَقَّ عَلَيۡهِمُ ٱلۡأَوۡلَيَٰنِ فَيُقۡسِمَانِ بِٱللَّهِ لَشَهَٰدَتُنَآ أَحَقُّ مِن شَهَٰدَتِهِمَا وَمَا ٱعۡتَدَيۡنَآ إِنَّآ إِذٗا لَّمِنَ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[المَائدة: 107]

Koma ngati zidziwika kuti anthu awiriwa ali ndi mlandu wina, sankhulani anthu ena awiri kuti aime m’malo mwawo, amene ali a chibale a munthu amene ali kufa. Iwo ayenera kulumbira pali Mulungu kuti: “Ife titsimikiza kuti umboni wathu ndi woona kuposa wa anthu awiriwo ndipo kuti ife sitinaperekepo umboni wabodza ndipo ngati ife tinama, ndiye kuti ndife olakwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فإن عثر على أنهما استحقا إثما فآخران يقومان مقامهما من الذين استحق, باللغة نيانجا

﴿فإن عثر على أنهما استحقا إثما فآخران يقومان مقامهما من الذين استحق﴾ [المَائدة: 107]

Khaled Ibrahim Betala
“Koma ngati kutaoneka kuti mboni ziwiri zija zanama pa umboni wawo, kapena zabisa chinthu, apo awiri achibale a wakufayo aimiire m’malo mwa mboni ziwirizo, (pambuyo pa Swala kuti aulule za bodza lawo). Choncho alumbilire m’dzina la Allah kuti: “Ndithu kulumbira kwathu nkoyenera kuvomerezedwa kuposa kulumbira kwawo; ndipo sitinapyole malire (mukulumbira kwathu). Ndipo sitikuzipekera mbonizo bodza. Ndithudi, ngati ife titachita zotere, ndiye kuti tikhala mwa ochita zoipa, (oyenera kulandira chilango cha Allah).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek