×

Koma chifukwa chakuti iwo adaphwanya lonjezo lawo, Ife tidawatemberera ndi kuumitsa mitima 5:13 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:13) ayat 13 in Chichewa

5:13 Surah Al-Ma’idah ayat 13 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 13 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿فَبِمَا نَقۡضِهِم مِّيثَٰقَهُمۡ لَعَنَّٰهُمۡ وَجَعَلۡنَا قُلُوبَهُمۡ قَٰسِيَةٗۖ يُحَرِّفُونَ ٱلۡكَلِمَ عَن مَّوَاضِعِهِۦ وَنَسُواْ حَظّٗا مِّمَّا ذُكِّرُواْ بِهِۦۚ وَلَا تَزَالُ تَطَّلِعُ عَلَىٰ خَآئِنَةٖ مِّنۡهُمۡ إِلَّا قَلِيلٗا مِّنۡهُمۡۖ فَٱعۡفُ عَنۡهُمۡ وَٱصۡفَحۡۚ إِنَّ ٱللَّهَ يُحِبُّ ٱلۡمُحۡسِنِينَ ﴾
[المَائدة: 13]

Koma chifukwa chakuti iwo adaphwanya lonjezo lawo, Ife tidawatemberera ndi kuumitsa mitima yawo. Iwo adasintha mawu ndi kuwachotsa m’malo mwake ndi kusiya zambiri zimene zidatumizidwa kwa iwo. Siudzasiya kuona ntchito za chinyengo mwa iwo kupatula owerengeka okha. Koma akhululukire ndipo uwalekerere. Ndithudi Mulungu amakonda anthu ochita zabwino

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فبما نقضهم ميثاقهم لعناهم وجعلنا قلوبهم قاسية يحرفون الكلم عن مواضعه ونسوا, باللغة نيانجا

﴿فبما نقضهم ميثاقهم لعناهم وجعلنا قلوبهم قاسية يحرفون الكلم عن مواضعه ونسوا﴾ [المَائدة: 13]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho chifukwa chakuswa pangano lawo, tidawatembelera; ndipo tidaumitsa mitima yawo. Ankasintha mawu (a Allah omwe adali m’mabuku a Taurat ndi Injili) kuwachotsa m’malo mwake ndipo adasiya kukwaniritsa gawo lalikulu la zomwe adakumbutsidwa. Ndipo ukhala ukuona (iwe Mtumiki {s.a.w}) chinyengo mwa ambiri a iwo, kupatula ochepa a iwo. Choncho akhululukire ndi kuwaleka. Ndithudi, Allah amakonda ochita zabwino
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek