×

Chifukwa cha chimenechi Ife tidakhazikitsa lamulo kwa ana a Israyeli kuti ngati 5:32 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:32) ayat 32 in Chichewa

5:32 Surah Al-Ma’idah ayat 32 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 32 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿مِنۡ أَجۡلِ ذَٰلِكَ كَتَبۡنَا عَلَىٰ بَنِيٓ إِسۡرَٰٓءِيلَ أَنَّهُۥ مَن قَتَلَ نَفۡسَۢا بِغَيۡرِ نَفۡسٍ أَوۡ فَسَادٖ فِي ٱلۡأَرۡضِ فَكَأَنَّمَا قَتَلَ ٱلنَّاسَ جَمِيعٗا وَمَنۡ أَحۡيَاهَا فَكَأَنَّمَآ أَحۡيَا ٱلنَّاسَ جَمِيعٗاۚ وَلَقَدۡ جَآءَتۡهُمۡ رُسُلُنَا بِٱلۡبَيِّنَٰتِ ثُمَّ إِنَّ كَثِيرٗا مِّنۡهُم بَعۡدَ ذَٰلِكَ فِي ٱلۡأَرۡضِ لَمُسۡرِفُونَ ﴾
[المَائدة: 32]

Chifukwa cha chimenechi Ife tidakhazikitsa lamulo kwa ana a Israyeli kuti ngati wina apha munthu mnzake osati chobwezera imfa ya wina kapena kuyambitsa chisokonezo pa dziko adzakhala ngati wapha anthu onse, ndipo kuti ngati wina adzapulumutsa moyo wa munthu, adzakhala ngati kuti adapulumutsa anthu onse. Ndithudi adabwera kwa iwo Atumwi athu ndi zizindikiro zooneka komabe sipanapite nthawi mmene ena a iwo adachimwa machimo akuluakulu m’dziko

❮ Previous Next ❯

ترجمة: من أجل ذلك كتبنا على بني إسرائيل أنه من قتل نفسا بغير, باللغة نيانجا

﴿من أجل ذلك كتبنا على بني إسرائيل أنه من قتل نفسا بغير﴾ [المَائدة: 32]

Khaled Ibrahim Betala
“Pachifukwa chazimenezo, tidawalamula ana a Israyeli kuti amene wapha munthu popanda iye (wophedwayo) kupha munthu, kapena kuchita chisokonezo pa dziko, ali ngati wapha anthu onse. Ndipo amene wamuleka munthu ali ndi moyo, ali ngati awapatsa moyo anthu onse. Ndithudi, atumiki Athu adawadzera iwo ndi zisonyezo zoonekera. Koma ndithu ambiri a iwo, pambuyo pa zimenezo, adapitirizabe kuononga pa dziko
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek