×

Ndipo motero weruza pakati pawo molingana ndi chivumbulutso cha Mulungu ndipo usatsatire 5:49 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:49) ayat 49 in Chichewa

5:49 Surah Al-Ma’idah ayat 49 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 49 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿وَأَنِ ٱحۡكُم بَيۡنَهُم بِمَآ أَنزَلَ ٱللَّهُ وَلَا تَتَّبِعۡ أَهۡوَآءَهُمۡ وَٱحۡذَرۡهُمۡ أَن يَفۡتِنُوكَ عَنۢ بَعۡضِ مَآ أَنزَلَ ٱللَّهُ إِلَيۡكَۖ فَإِن تَوَلَّوۡاْ فَٱعۡلَمۡ أَنَّمَا يُرِيدُ ٱللَّهُ أَن يُصِيبَهُم بِبَعۡضِ ذُنُوبِهِمۡۗ وَإِنَّ كَثِيرٗا مِّنَ ٱلنَّاسِ لَفَٰسِقُونَ ﴾
[المَائدة: 49]

Ndipo motero weruza pakati pawo molingana ndi chivumbulutso cha Mulungu ndipo usatsatire zilakolako zawo, ndipo chenjera nawo chifukwa akhoza kukubweza kugawo limene Mulungu wavumbulutsa kwa iwe. Koma ngati iwo akana chiweruzo chako, dziwani kuti chifuniro cha Mulungu ndi kuwalanga chifukwa cha zoipa zawo. Ndithudi anthu ambiri ndi oswa malamulo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وأن احكم بينهم بما أنـزل الله ولا تتبع أهواءهم واحذرهم أن يفتنوك, باللغة نيانجا

﴿وأن احكم بينهم بما أنـزل الله ولا تتبع أهواءهم واحذرهم أن يفتنوك﴾ [المَائدة: 49]

Khaled Ibrahim Betala
“Weruza pakati pawo ndi chimene Allah wavumbulutsa, ndipo usatsate zofuna zawo, koma chenjera nawo kuti angakusokoneze nkusiya zina mwa zimene Allah wavumbulutsa kwa iwe. Ndipo ngati anyozera dziwa kuti Allah afuna kuwapatsa chilango cha ena mwa machimo awo. Ndithudi, anthu ambiri ngopandukira (malamulo a Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek