×

Oh inu okhulupirira! Musapalane chibwenzi ndi anthu amene amachita chipongwe chipembedzo chanu 5:57 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:57) ayat 57 in Chichewa

5:57 Surah Al-Ma’idah ayat 57 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 57 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ لَا تَتَّخِذُواْ ٱلَّذِينَ ٱتَّخَذُواْ دِينَكُمۡ هُزُوٗا وَلَعِبٗا مِّنَ ٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡكِتَٰبَ مِن قَبۡلِكُمۡ وَٱلۡكُفَّارَ أَوۡلِيَآءَۚ وَٱتَّقُواْ ٱللَّهَ إِن كُنتُم مُّؤۡمِنِينَ ﴾
[المَائدة: 57]

Oh inu okhulupirira! Musapalane chibwenzi ndi anthu amene amachita chipongwe chipembedzo chanu ndi kuchisandutsa kukhala choseweretsa, amene ali pakati pa anthu amene adapatsidwa mau a Mulungu kale inu musanadze kapena anthu osakhulupirira ndipo opani Mulungu ngati inu ndinu anthu okhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا لا تتخذوا الذين اتخذوا دينكم هزوا ولعبا من الذين, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا لا تتخذوا الذين اتخذوا دينكم هزوا ولعبا من الذين﴾ [المَائدة: 57]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Musapalane nawo ubwenzi omwe akuchichitira chipongwe ndi masewera Chipembedzo chanu mwa omwe apatsidwa mabuku patsogolo panu, ndiponso mwa osakhulupirira, ndipo opani Allah ngati inu mulidi okhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek