×

Nena: “oh inu anthu a m’Buku! Kodi inu muli kutitsutsa ife chifukwa 5:59 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:59) ayat 59 in Chichewa

5:59 Surah Al-Ma’idah ayat 59 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 59 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿قُلۡ يَٰٓأَهۡلَ ٱلۡكِتَٰبِ هَلۡ تَنقِمُونَ مِنَّآ إِلَّآ أَنۡ ءَامَنَّا بِٱللَّهِ وَمَآ أُنزِلَ إِلَيۡنَا وَمَآ أُنزِلَ مِن قَبۡلُ وَأَنَّ أَكۡثَرَكُمۡ فَٰسِقُونَ ﴾
[المَائدة: 59]

Nena: “oh inu anthu a m’Buku! Kodi inu muli kutitsutsa ife chifukwa chakuti takhulupirira mwa Mulungu ndi mwa zimene zavumbulutsidwa kwa ife ndiponso zimene zidavumbulutsidwa kale ndipo kuti ambiri a inu ndinu anthu ochita zoipa?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قل ياأهل الكتاب هل تنقمون منا إلا أن آمنا بالله وما أنـزل, باللغة نيانجا

﴿قل ياأهل الكتاب هل تنقمون منا إلا أن آمنا بالله وما أنـزل﴾ [المَائدة: 59]

Khaled Ibrahim Betala
“Nena: “E inu anthu a buku! Kodi mukuona cholakwika kwa ife kaamba kakuti takhulupirira Allah ndi zomwe zavumbulutsidwa kwa ife ndi zomwenso zidavumbulutsidwa kale? Ndithudi, ambiri mwa inu ndi opandukira chilamulo (cha Allah).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek