×

Ndipo iwo akadatsatira Buku la chipangano chakale ndi chipangano chatsopano ndiponso zimene 5:66 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:66) ayat 66 in Chichewa

5:66 Surah Al-Ma’idah ayat 66 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 66 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿وَلَوۡ أَنَّهُمۡ أَقَامُواْ ٱلتَّوۡرَىٰةَ وَٱلۡإِنجِيلَ وَمَآ أُنزِلَ إِلَيۡهِم مِّن رَّبِّهِمۡ لَأَكَلُواْ مِن فَوۡقِهِمۡ وَمِن تَحۡتِ أَرۡجُلِهِمۚ مِّنۡهُمۡ أُمَّةٞ مُّقۡتَصِدَةٞۖ وَكَثِيرٞ مِّنۡهُمۡ سَآءَ مَا يَعۡمَلُونَ ﴾
[المَائدة: 66]

Ndipo iwo akadatsatira Buku la chipangano chakale ndi chipangano chatsopano ndiponso zimene zavumbulutsidwa kwa iwo kuchokera kwa Ambuye wawo, iwo akadadya zinthu kuchokera kumwamba ndi pansi pa miyendo yawo. Ena mwa iwo ndi anthu a chilungamo koma ambiri a iwo ndi ochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولو أنهم أقاموا التوراة والإنجيل وما أنـزل إليهم من ربهم لأكلوا من, باللغة نيانجا

﴿ولو أنهم أقاموا التوراة والإنجيل وما أنـزل إليهم من ربهم لأكلوا من﴾ [المَائدة: 66]

Khaled Ibrahim Betala
“Akadakhala kuti iwo adaigwiritsa ntchito Taurat ndi Injili, ndi zomwe zidavumbulutsidwa kwa iwo kuchokera kwa Mbuye wawo (monga Qurani), ndithudi akanadya za kumwamba ndi za pansi pa myendo yawo. Mwa iwo alipo amene akutsatira njira yabwino. Komanso ambiri mwa iwo nzoipa zedi zomwe akuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek