×

Iwo adali kuganiza kuti padalibe chilango chimene chikadawatsata, motero iwo adakhala a 5:71 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:71) ayat 71 in Chichewa

5:71 Surah Al-Ma’idah ayat 71 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 71 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿وَحَسِبُوٓاْ أَلَّا تَكُونَ فِتۡنَةٞ فَعَمُواْ وَصَمُّواْ ثُمَّ تَابَ ٱللَّهُ عَلَيۡهِمۡ ثُمَّ عَمُواْ وَصَمُّواْ كَثِيرٞ مِّنۡهُمۡۚ وَٱللَّهُ بَصِيرُۢ بِمَا يَعۡمَلُونَ ﴾
[المَائدة: 71]

Iwo adali kuganiza kuti padalibe chilango chimene chikadawatsata, motero iwo adakhala a khungu ndi osamva. Ndipo Mulungu adawakhululukira iwo komabe ambiri a iwo adali a khungu ndi osamva. Mulungu amaona zonse zimene akuchita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وحسبوا ألا تكون فتنة فعموا وصموا ثم تاب الله عليهم ثم عموا, باللغة نيانجا

﴿وحسبوا ألا تكون فتنة فعموا وصموا ثم تاب الله عليهم ثم عموا﴾ [المَائدة: 71]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ankaganiza kuti sipapezeka chilango; tero adali akhungu ndi agonthi. Kenako Allah adawalandira kulapa kwawo (pamene adalapa). Komabe ambiri a iwo adali akhungu, ndi ogontha. Ndipo Allah akuona zimene akuchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek