×

Ndithudi ndi osakhulupirira amene amati: “Mulungu ndi Messiya mwana wa mwamuna wa 5:72 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:72) ayat 72 in Chichewa

5:72 Surah Al-Ma’idah ayat 72 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 72 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿لَقَدۡ كَفَرَ ٱلَّذِينَ قَالُوٓاْ إِنَّ ٱللَّهَ هُوَ ٱلۡمَسِيحُ ٱبۡنُ مَرۡيَمَۖ وَقَالَ ٱلۡمَسِيحُ يَٰبَنِيٓ إِسۡرَٰٓءِيلَ ٱعۡبُدُواْ ٱللَّهَ رَبِّي وَرَبَّكُمۡۖ إِنَّهُۥ مَن يُشۡرِكۡ بِٱللَّهِ فَقَدۡ حَرَّمَ ٱللَّهُ عَلَيۡهِ ٱلۡجَنَّةَ وَمَأۡوَىٰهُ ٱلنَّارُۖ وَمَا لِلظَّٰلِمِينَ مِنۡ أَنصَارٖ ﴾
[المَائدة: 72]

Ndithudi ndi osakhulupirira amene amati: “Mulungu ndi Messiya mwana wa mwamuna wa Maria.” Koma Messiya mwini wake adati: “o inu ana a Israyeli! Pembedzani Mulungu, Ambuye wanga amene ndi Ambuye wanu.”Ndithudi aliyense amene apembedza milungu ina m’malo mwa Mulungu yekha sadzalowa ku Paradiso ndipo malo ake ndi kumoto. Ndipo anthu ochita zoipa alibe owathandiza

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لقد كفر الذين قالوا إن الله هو المسيح ابن مريم وقال المسيح, باللغة نيانجا

﴿لقد كفر الذين قالوا إن الله هو المسيح ابن مريم وقال المسيح﴾ [المَائدة: 72]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi am’kana Allah amene anena kuti, Mulungu ndiye Isa (Yesu) mwana wa Mariya.” Pomwe Mesiya adati: “Inu ana a Israyeli! Pembedzani Allah Yemwe ndi Mbuye wanga ndiponso Mbuye wanu.” Ndithudi, amene aphatikize Allah ndi chinthu china, ndithudi Allah waletsa kwa iye kukalowa ku Munda wamtendere, ndipo malo ake ndi ku Moto. Ndipo anthu ochita zoipa sadzakhala ndi athandizi
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek