×

Iwe umawaona anthu ambiri akupalana ubwenzi ndi anthu osakhulupirira. Ndithudi ndi zinthu 5:80 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Ma’idah ⮕ (5:80) ayat 80 in Chichewa

5:80 Surah Al-Ma’idah ayat 80 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Ma’idah ayat 80 - المَائدة - Page - Juz 6

﴿تَرَىٰ كَثِيرٗا مِّنۡهُمۡ يَتَوَلَّوۡنَ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْۚ لَبِئۡسَ مَا قَدَّمَتۡ لَهُمۡ أَنفُسُهُمۡ أَن سَخِطَ ٱللَّهُ عَلَيۡهِمۡ وَفِي ٱلۡعَذَابِ هُمۡ خَٰلِدُونَ ﴾
[المَائدة: 80]

Iwe umawaona anthu ambiri akupalana ubwenzi ndi anthu osakhulupirira. Ndithudi ndi zinthu zoipa zimene iwo adatsogoza ndipo chifukwa cha ichi mkwiyo wa Mulungu unagwa pa iwo ndipo adzalandira chilango chosatha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ترى كثيرا منهم يتولون الذين كفروا لبئس ما قدمت لهم أنفسهم أن, باللغة نيانجا

﴿ترى كثيرا منهم يتولون الذين كفروا لبئس ما قدمت لهم أنفسهم أن﴾ [المَائدة: 80]

Khaled Ibrahim Betala
“Uwaona ambiri a iwo akupalana ubwenzi ndi omwe sadakhulupirire Allah, (opembedza mafano ndi cholinga chomenya nkhondo chipembedzo cha Chisilamu). Nzoipa kwambiri zomwe adadzitsogozera okha. Tero Allah adawakwiira ndipo m’masautso adzakhalamo nthawi yaitali
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek