×

Kodi nthawi siinakwane yoti okhulupirira enieni apereke mitima yawo modzichepetsa ndipo kuti 57:16 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-hadid ⮕ (57:16) ayat 16 in Chichewa

57:16 Surah Al-hadid ayat 16 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-hadid ayat 16 - الحدِيد - Page - Juz 27

﴿۞ أَلَمۡ يَأۡنِ لِلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ أَن تَخۡشَعَ قُلُوبُهُمۡ لِذِكۡرِ ٱللَّهِ وَمَا نَزَلَ مِنَ ٱلۡحَقِّ وَلَا يَكُونُواْ كَٱلَّذِينَ أُوتُواْ ٱلۡكِتَٰبَ مِن قَبۡلُ فَطَالَ عَلَيۡهِمُ ٱلۡأَمَدُ فَقَسَتۡ قُلُوبُهُمۡۖ وَكَثِيرٞ مِّنۡهُمۡ فَٰسِقُونَ ﴾
[الحدِيد: 16]

Kodi nthawi siinakwane yoti okhulupirira enieni apereke mitima yawo modzichepetsa ndipo kuti azikumbukira Mulungu ndi choonadi chimene chavumbulutsidwa kwa iwo ndipo kuti asakhale ngati iwo amene adapatsidwa Buku nthawi ya kale? Koma patapita nthawi, mitima yawo idalimba. Ndipo ambiri a iwo ndi ophwanya malamulo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ألم يأن للذين آمنوا أن تخشع قلوبهم لذكر الله وما نـزل من, باللغة نيانجا

﴿ألم يأن للذين آمنوا أن تخشع قلوبهم لذكر الله وما نـزل من﴾ [الحدِيد: 16]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi siidakwane nthawi kwa okhulupirira kuti mitima yawo idzichepetse pokumbukira Allah ndi zomwe zidavumbulutsidwa za chowonadi (Qur’an yolemekezeka)? Ndi kuti asakhale monga omwe adapatsidwa buku kale (Ayuda ndi Akhrisitu) amene nthawi yawo yosiyana ndi aneneri awo idali yaitali. Choncho mitima yawo idauma ndipo ambiri a iwo adatuluka m’chilamulo (cha Allah)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek