×

Ndipo ena akazi anu amene adasiya kupita kumwezi, kwa iwo nthawi yawo 65:4 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah AT-Talaq ⮕ (65:4) ayat 4 in Chichewa

65:4 Surah AT-Talaq ayat 4 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah AT-Talaq ayat 4 - الطَّلَاق - Page - Juz 28

﴿وَٱلَّٰٓـِٔي يَئِسۡنَ مِنَ ٱلۡمَحِيضِ مِن نِّسَآئِكُمۡ إِنِ ٱرۡتَبۡتُمۡ فَعِدَّتُهُنَّ ثَلَٰثَةُ أَشۡهُرٖ وَٱلَّٰٓـِٔي لَمۡ يَحِضۡنَۚ وَأُوْلَٰتُ ٱلۡأَحۡمَالِ أَجَلُهُنَّ أَن يَضَعۡنَ حَمۡلَهُنَّۚ وَمَن يَتَّقِ ٱللَّهَ يَجۡعَل لَّهُۥ مِنۡ أَمۡرِهِۦ يُسۡرٗا ﴾
[الطَّلَاق: 4]

Ndipo ena akazi anu amene adasiya kupita kumwezi, kwa iwo nthawi yawo yodikira, ngati inu mukaika, ndi miyezi itatu ndipo iwo amene anasiyiratu, nthawi yawo idzakhala chimodzimodzi. Ndipo iwo amene ali ndi akazi odwala pakati, nthawi yawo idzakhala mpaka pamene abereka. Ndipo aliyense amene amaopa Mulungu, Iye adzamuchepetsera mavuto ake

❮ Previous Next ❯

ترجمة: واللائي يئسن من المحيض من نسائكم إن ارتبتم فعدتهن ثلاثة أشهر واللائي, باللغة نيانجا

﴿واللائي يئسن من المحيض من نسائكم إن ارتبتم فعدتهن ثلاثة أشهر واللائي﴾ [الطَّلَاق: 4]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo Edda ya amene asiya kudwala kumwezi mwa akazi anu chifukwa cha kukula, ngati mukukaika (nthawi ya Edda yawo), Edda yawo ndi miyezi itatu. Ndi omwe sadathe nsinkhu Edda yawo ndi momwemonso. Tsono akazi apakati nthawi yothera Edda yawo ndipomwe abereka. Ndipo amene aopa Allah amfewetsera zinthu zake (kuti zikhale zosavuta)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek