×

Ndipo Iye adzamupatsa zinthu kuchokera ku mbali imene sanali kuyembekeza. Ndipo aliyense 65:3 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah AT-Talaq ⮕ (65:3) ayat 3 in Chichewa

65:3 Surah AT-Talaq ayat 3 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah AT-Talaq ayat 3 - الطَّلَاق - Page - Juz 28

﴿وَيَرۡزُقۡهُ مِنۡ حَيۡثُ لَا يَحۡتَسِبُۚ وَمَن يَتَوَكَّلۡ عَلَى ٱللَّهِ فَهُوَ حَسۡبُهُۥٓۚ إِنَّ ٱللَّهَ بَٰلِغُ أَمۡرِهِۦۚ قَدۡ جَعَلَ ٱللَّهُ لِكُلِّ شَيۡءٖ قَدۡرٗا ﴾
[الطَّلَاق: 3]

Ndipo Iye adzamupatsa zinthu kuchokera ku mbali imene sanali kuyembekeza. Ndipo aliyense amene amakhulupirira mwa Mulungu, Iye adzamupatsa chili chonse. Mulungu, ndithudi, adzamupatsa iye zofuna zake zonse. Ndithudi Mulungu adakhazikitsa muyeso wa chilichonse

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ويرزقه من حيث لا يحتسب ومن يتوكل على الله فهو حسبه إن, باللغة نيانجا

﴿ويرزقه من حيث لا يحتسب ومن يتوكل على الله فهو حسبه إن﴾ [الطَّلَاق: 3]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo ampatsa rizq kuchokera momwe samayembekezeramo. Ndipo amene akutsamira kwa Allah (pa zinthu zake zonse), ndiye kuti Allah ali wokwana kwa iye (kumkonzera chilichonse), ndithu Allah Ngokwaniritsa cholinga Chake ndi chofuna Chake. Ndithu chinthu chilichonse Allah wachipatsa mlingo wake woyenera (ndipo sichingaupyole)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek