×

Mulungu ali kupereka chitsanzo kwa anthu osakhulupirira cha nkhani ya mkazi wa 66:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Tahrim ⮕ (66:10) ayat 10 in Chichewa

66:10 Surah At-Tahrim ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Tahrim ayat 10 - التَّحرِيم - Page - Juz 28

﴿ضَرَبَ ٱللَّهُ مَثَلٗا لِّلَّذِينَ كَفَرُواْ ٱمۡرَأَتَ نُوحٖ وَٱمۡرَأَتَ لُوطٖۖ كَانَتَا تَحۡتَ عَبۡدَيۡنِ مِنۡ عِبَادِنَا صَٰلِحَيۡنِ فَخَانَتَاهُمَا فَلَمۡ يُغۡنِيَا عَنۡهُمَا مِنَ ٱللَّهِ شَيۡـٔٗا وَقِيلَ ٱدۡخُلَا ٱلنَّارَ مَعَ ٱلدَّٰخِلِينَ ﴾
[التَّحرِيم: 10]

Mulungu ali kupereka chitsanzo kwa anthu osakhulupirira cha nkhani ya mkazi wa Nowa ndi mkazi wa Loti. Iwo adali akazi a Atumiki athu awiri a ngwiro, koma onse adanyenga amuna awo. Iwo sadalandire kuchokera kwa Mulungu chabwino china chilichonse chifukwa chamakhalidwe awo. Koma iwo adauzidwa kuti: “Lowani inu kumoto pamodzi ndi ena amene ali kulowako.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ضرب الله مثلا للذين كفروا امرأة نوح وامرأة لوط كانتا تحت عبدين, باللغة نيانجا

﴿ضرب الله مثلا للذين كفروا امرأة نوح وامرأة لوط كانتا تحت عبدين﴾ [التَّحرِيم: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Allah wapereka fanizo la osakhulupirira monga mkazi wa Nuh ndi mkazi wa Luti. Awiriwa adali pansi pa akapolo Athu awiri abwino, koma adali osakhulupirika kwa amuna awo, (ndipo amuna awo) sadawateteze kalikonse ku chilango cha Allah, ndipo kudanenedwa kwa iwo “Lowani ku Moto pamodzi (ndi ena) olowa.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek