×

Ndipo Mulungu wapereka chitsanzo kwa anthu okhulupirira, nkhani ya mkazi wa Farao. 66:11 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Tahrim ⮕ (66:11) ayat 11 in Chichewa

66:11 Surah At-Tahrim ayat 11 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Tahrim ayat 11 - التَّحرِيم - Page - Juz 28

﴿وَضَرَبَ ٱللَّهُ مَثَلٗا لِّلَّذِينَ ءَامَنُواْ ٱمۡرَأَتَ فِرۡعَوۡنَ إِذۡ قَالَتۡ رَبِّ ٱبۡنِ لِي عِندَكَ بَيۡتٗا فِي ٱلۡجَنَّةِ وَنَجِّنِي مِن فِرۡعَوۡنَ وَعَمَلِهِۦ وَنَجِّنِي مِنَ ٱلۡقَوۡمِ ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[التَّحرِيم: 11]

Ndipo Mulungu wapereka chitsanzo kwa anthu okhulupirira, nkhani ya mkazi wa Farao. Pamene iye adati: “oh Ambuye wanga! Ndimangireni pafupi ndi Inu, nyumba ya ulemu ku Paradiso, ndipo ndipulumutseni kwa Farao ndi ntchito zake ndipo ndipulumutseni ine kwa athu amene amachita zoipa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وضرب الله مثلا للذين آمنوا امرأة فرعون إذ قالت رب ابن لي, باللغة نيانجا

﴿وضرب الله مثلا للذين آمنوا امرأة فرعون إذ قالت رب ابن لي﴾ [التَّحرِيم: 11]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndiponso Allah wapereka fanizo la amene akhulupirira monga mkazi wa Firiauna (Farawo) pamene adanena: “Mbuye wanga! Ndimangireni kwa inu Nyumba mu Jannah, ndipo ndipulumutseni kwa Firiauna ndi zochita zake, ndiponso ndipulumutseni kwa anthu oipa (ndi amtopola.)”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek