×

Pafupifupi kuphulika chifukwa cha kukwiya. Ndipo nthawi zonse pamene gulu liponyedwamo, amene 67:8 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Mulk ⮕ (67:8) ayat 8 in Chichewa

67:8 Surah Al-Mulk ayat 8 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Mulk ayat 8 - المُلك - Page - Juz 29

﴿تَكَادُ تَمَيَّزُ مِنَ ٱلۡغَيۡظِۖ كُلَّمَآ أُلۡقِيَ فِيهَا فَوۡجٞ سَأَلَهُمۡ خَزَنَتُهَآ أَلَمۡ يَأۡتِكُمۡ نَذِيرٞ ﴾
[المُلك: 8]

Pafupifupi kuphulika chifukwa cha kukwiya. Ndipo nthawi zonse pamene gulu liponyedwamo, amene amayang’anira moto adzafunsa kuti: “Kodi panalibe wina aliyense amene adadza kwa inu kudzakuchenjezani?”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: تكاد تميز من الغيظ كلما ألقي فيها فوج سألهم خزنتها ألم يأتكم, باللغة نيانجا

﴿تكاد تميز من الغيظ كلما ألقي فيها فوج سألهم خزنتها ألم يأتكم﴾ [المُلك: 8]

Khaled Ibrahim Betala
“Udzayandikira kudukaduka chifukwa cha mkwiyo (kukwiira oipa); nthawi iliyonse gulu (la oipa) likadzaponyedwa m’menemo, Angelo oyang’anira Motowo adzawafunsa (mowadzudzula): “Kodi sadakufikeni mchenjezi (wokuchenjezani za tsikuli?).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek