×

Ndipo Ife tidakupatsani ulamuliro padziko ndipo tidakuikirani zofunikira mu moyo wanu koma 7:10 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:10) ayat 10 in Chichewa

7:10 Surah Al-A‘raf ayat 10 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 10 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَلَقَدۡ مَكَّنَّٰكُمۡ فِي ٱلۡأَرۡضِ وَجَعَلۡنَا لَكُمۡ فِيهَا مَعَٰيِشَۗ قَلِيلٗا مَّا تَشۡكُرُونَ ﴾
[الأعرَاف: 10]

Ndipo Ife tidakupatsani ulamuliro padziko ndipo tidakuikirani zofunikira mu moyo wanu koma kuthokoza kwanu ndi kochepa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ولقد مكناكم في الأرض وجعلنا لكم فيها معايش قليلا ما تشكرون, باللغة نيانجا

﴿ولقد مكناكم في الأرض وجعلنا لكم فيها معايش قليلا ما تشكرون﴾ [الأعرَاف: 10]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndithudi tinakupatsani mphamvu yokhalira pa dziko, ndipo takupangirani m’menemo zinthu zofunika pa moyo wanu. Koma kuyamika kwanu mpang’ono
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek