Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 105 - الأعرَاف - Page - Juz 9
﴿حَقِيقٌ عَلَىٰٓ أَن لَّآ أَقُولَ عَلَى ٱللَّهِ إِلَّا ٱلۡحَقَّۚ قَدۡ جِئۡتُكُم بِبَيِّنَةٖ مِّن رَّبِّكُمۡ فَأَرۡسِلۡ مَعِيَ بَنِيٓ إِسۡرَٰٓءِيلَ ﴾
[الأعرَاف: 105]
﴿حقيق على أن لا أقول على الله إلا الحق قد جئتكم ببينة﴾ [الأعرَاف: 105]
Khaled Ibrahim Betala ““Ndikofunika kwa ine kuti ndisamnenere Allah chilichonse koma choonadi basi. Ndithu ndakudzerani ndi chizindikiro choonekera kuchokera kwa Mbuye wanu. Choncho, aleke ndinke nawo ana a Israyeli.” |