×

Iwo adati: “Bamusungani pa kanthawi, iye pamodzi ndi m’bale wake ndipo tumizani 7:111 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:111) ayat 111 in Chichewa

7:111 Surah Al-A‘raf ayat 111 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 111 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿قَالُوٓاْ أَرۡجِهۡ وَأَخَاهُ وَأَرۡسِلۡ فِي ٱلۡمَدَآئِنِ حَٰشِرِينَ ﴾
[الأعرَاف: 111]

Iwo adati: “Bamusungani pa kanthawi, iye pamodzi ndi m’bale wake ndipo tumizani anthu ku mizinda kuti akasonkhanitse.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالوا أرجه وأخاه وأرسل في المدائن حاشرين, باللغة نيانجا

﴿قالوا أرجه وأخاه وأرسل في المدائن حاشرين﴾ [الأعرَاف: 111]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iwo) adati (kwa Farawo): “Muleke pang’ono iye ndi m’bale wakeyu (usawaphe); ndipo tumiza osonkhanitsa m’mizinda kuti akusonkhanitsire (amatsenga onse akuluakulu).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek