×

Iwo adati, “Ife tidali kuzunzidwa iwe usadadze kwa ife ndipo tikuzunzidwabe pamene 7:129 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:129) ayat 129 in Chichewa

7:129 Surah Al-A‘raf ayat 129 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 129 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿قَالُوٓاْ أُوذِينَا مِن قَبۡلِ أَن تَأۡتِيَنَا وَمِنۢ بَعۡدِ مَا جِئۡتَنَاۚ قَالَ عَسَىٰ رَبُّكُمۡ أَن يُهۡلِكَ عَدُوَّكُمۡ وَيَسۡتَخۡلِفَكُمۡ فِي ٱلۡأَرۡضِ فَيَنظُرَ كَيۡفَ تَعۡمَلُونَ ﴾
[الأعرَاف: 129]

Iwo adati, “Ife tidali kuzunzidwa iwe usadadze kwa ife ndipo tikuzunzidwabe pamene iwe wadza.” Iye adati: “Mwina Ambuye wanu akhoza kuwononga adani anu ndi kukupangani inu kukhala olamulira m’dziko kuti Iye aone mmene muzidzachitira.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قالوا أوذينا من قبل أن تأتينا ومن بعد ما جئتنا قال عسى, باللغة نيانجا

﴿قالوا أوذينا من قبل أن تأتينا ومن بعد ما جئتنا قال عسى﴾ [الأعرَاف: 129]

Khaled Ibrahim Betala
“(Iwo) adati: “Takhala tikuzunzidwa usanatidzere ndiponso (tsopano) pamene watidzera.” (Mûsa) adati: “Mwina Mbuye wanu amuononga mdani wanu ndipo akuchitani kukhala alowammalo m’dzikoli, ndi kuti aone mmene mungachitire.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek