×

Ine ndidzawabisila zizindikiro zanga anthu a odzikweza ndi ochita zoipa mopanda chilungamo 7:146 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:146) ayat 146 in Chichewa

7:146 Surah Al-A‘raf ayat 146 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 146 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿سَأَصۡرِفُ عَنۡ ءَايَٰتِيَ ٱلَّذِينَ يَتَكَبَّرُونَ فِي ٱلۡأَرۡضِ بِغَيۡرِ ٱلۡحَقِّ وَإِن يَرَوۡاْ كُلَّ ءَايَةٖ لَّا يُؤۡمِنُواْ بِهَا وَإِن يَرَوۡاْ سَبِيلَ ٱلرُّشۡدِ لَا يَتَّخِذُوهُ سَبِيلٗا وَإِن يَرَوۡاْ سَبِيلَ ٱلۡغَيِّ يَتَّخِذُوهُ سَبِيلٗاۚ ذَٰلِكَ بِأَنَّهُمۡ كَذَّبُواْ بِـَٔايَٰتِنَا وَكَانُواْ عَنۡهَا غَٰفِلِينَ ﴾
[الأعرَاف: 146]

Ine ndidzawabisila zizindikiro zanga anthu a odzikweza ndi ochita zoipa mopanda chilungamo padziko ngakhale kuti iwo ataona chizindikiro china chilichonse, sadzachikhulupirira. Ngati aona njira yoyenera, iwo sadzaitsata, koma akaona njira yopotoka, iwo adzaitsatira iyo; chifukwa chakuti iwo adakana zizindikiro zathu ndipo sadafune kuzimvera ayi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: سأصرف عن آياتي الذين يتكبرون في الأرض بغير الحق وإن يروا كل, باللغة نيانجا

﴿سأصرف عن آياتي الذين يتكبرون في الأرض بغير الحق وإن يروا كل﴾ [الأعرَاف: 146]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndiwatembenuzira kuzilingalira zizindikiro Zanga awo omwe akudzitukumula pa dziko popanda choonadi, ndipo akaona chizindikiro chilichonse sachikhulupirira, ndipo akaona njira yolungama sakuiyesa njira (sakuitsata), koma akaona njira yosokera akuiyetsa njira (akuitsata). Zimenezo nchifukwa chakuti iwo adatsutsa zizindikiro Zathu ndipo anali osazilabadira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek