×

Ndipo afunse iwo za Mzinda umene udali pa mbali pa nyanja pamene 7:163 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:163) ayat 163 in Chichewa

7:163 Surah Al-A‘raf ayat 163 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 163 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿وَسۡـَٔلۡهُمۡ عَنِ ٱلۡقَرۡيَةِ ٱلَّتِي كَانَتۡ حَاضِرَةَ ٱلۡبَحۡرِ إِذۡ يَعۡدُونَ فِي ٱلسَّبۡتِ إِذۡ تَأۡتِيهِمۡ حِيتَانُهُمۡ يَوۡمَ سَبۡتِهِمۡ شُرَّعٗا وَيَوۡمَ لَا يَسۡبِتُونَ لَا تَأۡتِيهِمۡۚ كَذَٰلِكَ نَبۡلُوهُم بِمَا كَانُواْ يَفۡسُقُونَ ﴾
[الأعرَاف: 163]

Ndipo afunse iwo za Mzinda umene udali pa mbali pa nyanja pamene iwo adaphwanya malamulo a tsiku la Sabata pamene nsomba zinali kusewera pafupi ndi kumatulutsa mitu yawo pamene sizidali kutero pa masiku ena. Motero Ife tidawayesa chifukwa iwo adali anthu oswa malamulo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: واسألهم عن القرية التي كانت حاضرة البحر إذ يعدون في السبت إذ, باللغة نيانجا

﴿واسألهم عن القرية التي كانت حاضرة البحر إذ يعدون في السبت إذ﴾ [الأعرَاف: 163]

Khaled Ibrahim Betala
“Tawafunsani nkhani ya mudzi umene udali m’mphepete mwa nyanja; (anthu am’mudziwo) pamene adali kuswa (lamulo la) tsiku la Sabata (lomwe adauzidwa kuti pa tsikuli asamachite usodzi wa nsomba, koma m’malo mwake azichita mapemphero okha). Nsomba zawo zinkawadzera yandayanda patsiku la Sabata, koma patsiku lomwe silidali la Sabata sizidali kuwabwerera (yandayanda). Motero tidawayesa mayeso chifukwa chakuchimwa kwawo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek