×

Ndi pamene gulu lina lidati, “Kodi ndi chifukwa chiyani uli kulalikira kwa 7:164 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:164) ayat 164 in Chichewa

7:164 Surah Al-A‘raf ayat 164 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 164 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿وَإِذۡ قَالَتۡ أُمَّةٞ مِّنۡهُمۡ لِمَ تَعِظُونَ قَوۡمًا ٱللَّهُ مُهۡلِكُهُمۡ أَوۡ مُعَذِّبُهُمۡ عَذَابٗا شَدِيدٗاۖ قَالُواْ مَعۡذِرَةً إِلَىٰ رَبِّكُمۡ وَلَعَلَّهُمۡ يَتَّقُونَ ﴾
[الأعرَاف: 164]

Ndi pamene gulu lina lidati, “Kodi ndi chifukwa chiyani uli kulalikira kwa anthu amene Mulungu ali pafupi kuwaononga kapena kuwalanga kwambiri?” Iwo adayankha kuti; “Ife tisadzakhale ndi mlandu kwa Ambuye wanu ndiponso kuti mwina iwo angaope Mulungu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ قالت أمة منهم لم تعظون قوما الله مهلكهم أو معذبهم عذابا, باللغة نيانجا

﴿وإذ قالت أمة منهم لم تعظون قوما الله مهلكهم أو معذبهم عذابا﴾ [الأعرَاف: 164]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (akumbutse ) pamene gulu lina mwa iwo linkanena (kwa omwe amachenjeza amene adaswa kupatulika kwa tsiku la Sabata pamene adati): “Pali phindu lanji kuwachenjeza anthu omwe Allah awawononga kapena kuwalanga ndi chilango chaukali pompano pa dziko lapansi)? (Iwo) adati: “Kuti tidzakhale ndi chidandaulo kwa Mbuye wathu (ponena kuti tidawachenjeza koma sadatimvere) ndi kutinso mwina angaope (Allah nasiya kuswa lamulo Lake).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek