×

Ndipo pamaso pa iwo amene adaiwala chikumbutso chimene chidaperekedwa kwa iwo, Ife 7:165 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:165) ayat 165 in Chichewa

7:165 Surah Al-A‘raf ayat 165 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 165 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿فَلَمَّا نَسُواْ مَا ذُكِّرُواْ بِهِۦٓ أَنجَيۡنَا ٱلَّذِينَ يَنۡهَوۡنَ عَنِ ٱلسُّوٓءِ وَأَخَذۡنَا ٱلَّذِينَ ظَلَمُواْ بِعَذَابِۭ بَـِٔيسِۭ بِمَا كَانُواْ يَفۡسُقُونَ ﴾
[الأعرَاف: 165]

Ndipo pamaso pa iwo amene adaiwala chikumbutso chimene chidaperekedwa kwa iwo, Ife tidapulumutsa iwo amene amaletsa zoipa ndipo Ife tidawalanga amene adali olakwa ndi chilango chowawa chifukwa cha machimo awo

❮ Previous Next ❯

ترجمة: فلما نسوا ما ذكروا به أنجينا الذين ينهون عن السوء وأخذنا الذين, باللغة نيانجا

﴿فلما نسوا ما ذكروا به أنجينا الذين ينهون عن السوء وأخذنا الذين﴾ [الأعرَاف: 165]

Khaled Ibrahim Betala
“Choncho, pamene sanalabadire zimene anauzidwa ndi kuchenjezedwa, tinawapulumutsa (anthu) omwe amaletsa zoipa, ndipo tidawakhaulitsa amene ankadzichitira okha zoipa ndi chilango choipa kwambiri chifukwa chakupandukila (kwawo) malamulo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek