×

Wawo adzakhala kama wa moto ndipo pamwamba pawo padzakhala malawi a moto. 7:41 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:41) ayat 41 in Chichewa

7:41 Surah Al-A‘raf ayat 41 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 41 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿لَهُم مِّن جَهَنَّمَ مِهَادٞ وَمِن فَوۡقِهِمۡ غَوَاشٖۚ وَكَذَٰلِكَ نَجۡزِي ٱلظَّٰلِمِينَ ﴾
[الأعرَاف: 41]

Wawo adzakhala kama wa moto ndipo pamwamba pawo padzakhala malawi a moto. M’menemo ndi m’mene tidzawalipirira anthu ochita zoipa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لهم من جهنم مهاد ومن فوقهم غواش وكذلك نجزي الظالمين, باللغة نيانجا

﴿لهم من جهنم مهاد ومن فوقهم غواش وكذلك نجزي الظالمين﴾ [الأعرَاف: 41]

Khaled Ibrahim Betala
“Moto wa Jahannam ndi mphasa yawo; ndipo pamwamba pawo adzakhala ndi (chofunda cha Moto) chowaphimba. Umo ndimomwe Tikuwalipirira anthu osalungama
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek