×

Koma iwo amene anakhulupirira ndipo amachita ntchito zabwino; Ife sitisenzetsa munthu katundu 7:42 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:42) ayat 42 in Chichewa

7:42 Surah Al-A‘raf ayat 42 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 42 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَٱلَّذِينَ ءَامَنُواْ وَعَمِلُواْ ٱلصَّٰلِحَٰتِ لَا نُكَلِّفُ نَفۡسًا إِلَّا وُسۡعَهَآ أُوْلَٰٓئِكَ أَصۡحَٰبُ ٱلۡجَنَّةِۖ هُمۡ فِيهَا خَٰلِدُونَ ﴾
[الأعرَاف: 42]

Koma iwo amene anakhulupirira ndipo amachita ntchito zabwino; Ife sitisenzetsa munthu katundu amene sangathe kumunyamula; iwo ndi anthu a ku Paradiso. Ndipo adzakhalako mpaka kalekale

❮ Previous Next ❯

ترجمة: والذين آمنوا وعملوا الصالحات لا نكلف نفسا إلا وسعها أولئك أصحاب الجنة, باللغة نيانجا

﴿والذين آمنوا وعملوا الصالحات لا نكلف نفسا إلا وسعها أولئك أصحاب الجنة﴾ [الأعرَاف: 42]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo amene akhulupirira ndikumachita zabwino, sitikakamiza munthu aliyense koma chimene angachithe, awo ndiwo anthu a ku Munda wamtendere. M’menemo iwo akakhala nthawi yaitali
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek