×

“Iwo amene adasandutsa chipembedzo chawo ngatinthabwalandichoseweretsandipoadalikunyengedwa ndi zokoma za m’moyo wa padziko 7:51 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:51) ayat 51 in Chichewa

7:51 Surah Al-A‘raf ayat 51 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 51 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿ٱلَّذِينَ ٱتَّخَذُواْ دِينَهُمۡ لَهۡوٗا وَلَعِبٗا وَغَرَّتۡهُمُ ٱلۡحَيَوٰةُ ٱلدُّنۡيَاۚ فَٱلۡيَوۡمَ نَنسَىٰهُمۡ كَمَا نَسُواْ لِقَآءَ يَوۡمِهِمۡ هَٰذَا وَمَا كَانُواْ بِـَٔايَٰتِنَا يَجۡحَدُونَ ﴾
[الأعرَاف: 51]

“Iwo amene adasandutsa chipembedzo chawo ngatinthabwalandichoseweretsandipoadalikunyengedwa ndi zokoma za m’moyo wa padziko lapansi. Motero lero Ife tiwaiwala monga mmene adaiwalira za kukumana kwa tsiku lawoli ndi chifukwa chokana zizindikiro zathu.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الذين اتخذوا دينهم لهوا ولعبا وغرتهم الحياة الدنيا فاليوم ننساهم كما نسوا, باللغة نيانجا

﴿الذين اتخذوا دينهم لهوا ولعبا وغرتهم الحياة الدنيا فاليوم ننساهم كما نسوا﴾ [الأعرَاف: 51]

Khaled Ibrahim Betala
“Omwe adachita chipembedzo chawo kukhala zinthu zopanda pake ndiponso masewero; ndipo udawanyenga moyo wa m’dziko. Choncho, lero Ifenso tiwaiwala (tiwaleka ku Moto) monga momwe adakuiwalira kukumana ndi tsiku lawo ili, ndi chifukwa chakukana kwawo zivumbulutso Zathu
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek