×

Atsogoleri a anthu amene amadzikweza mu anthu ake anati kwa anthu ofoka 7:75 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:75) ayat 75 in Chichewa

7:75 Surah Al-A‘raf ayat 75 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 75 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿قَالَ ٱلۡمَلَأُ ٱلَّذِينَ ٱسۡتَكۡبَرُواْ مِن قَوۡمِهِۦ لِلَّذِينَ ٱسۡتُضۡعِفُواْ لِمَنۡ ءَامَنَ مِنۡهُمۡ أَتَعۡلَمُونَ أَنَّ صَٰلِحٗا مُّرۡسَلٞ مِّن رَّبِّهِۦۚ قَالُوٓاْ إِنَّا بِمَآ أُرۡسِلَ بِهِۦ مُؤۡمِنُونَ ﴾
[الأعرَاف: 75]

Atsogoleri a anthu amene amadzikweza mu anthu ake anati kwa anthu ofoka amene adakhulupirira mwa iwo: “Kodi mukudziwa kuti Saleh ndi wotumidwa kuchokera kwa Ambuye wake?” Iwo adati: “Ndithudi ife takhulupirira mzimene iye watumidwa.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: قال الملأ الذين استكبروا من قومه للذين استضعفوا لمن آمن منهم أتعلمون, باللغة نيانجا

﴿قال الملأ الذين استكبروا من قومه للذين استضعفوا لمن آمن منهم أتعلمون﴾ [الأعرَاف: 75]

Khaled Ibrahim Betala
“Adanena akuluakulu omwe adali odzitukumula mwa anthu ake kuuza omwe adaponderezedwa kwa amene adakhulupirira mwa iwo: “Kodi muli ndi chitsimikizo kuti Swalih ngotumizidwa ndi Mbuye Wake (wapatsidwa utumiki)?” (Iwo) Adati: “Ndithu ife tikukhulupirira zomwe watumidwa nazo (kuzifikitsa kwa ife).”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek