×

Kwa anthu a ku Midiyani tidatumiza m’bale wawo Shaibu. Iye anati: “Oh 7:85 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:85) ayat 85 in Chichewa

7:85 Surah Al-A‘raf ayat 85 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 85 - الأعرَاف - Page - Juz 8

﴿وَإِلَىٰ مَدۡيَنَ أَخَاهُمۡ شُعَيۡبٗاۚ قَالَ يَٰقَوۡمِ ٱعۡبُدُواْ ٱللَّهَ مَا لَكُم مِّنۡ إِلَٰهٍ غَيۡرُهُۥۖ قَدۡ جَآءَتۡكُم بَيِّنَةٞ مِّن رَّبِّكُمۡۖ فَأَوۡفُواْ ٱلۡكَيۡلَ وَٱلۡمِيزَانَ وَلَا تَبۡخَسُواْ ٱلنَّاسَ أَشۡيَآءَهُمۡ وَلَا تُفۡسِدُواْ فِي ٱلۡأَرۡضِ بَعۡدَ إِصۡلَٰحِهَاۚ ذَٰلِكُمۡ خَيۡرٞ لَّكُمۡ إِن كُنتُم مُّؤۡمِنِينَ ﴾
[الأعرَاف: 85]

Kwa anthu a ku Midiyani tidatumiza m’bale wawo Shaibu. Iye anati: “Oh anthu anga! Pembedzani Mulungu, inu mulibe mulungu wina koma Iye yekha. Ndithudi chizindikiro chooneka chadza kwa inu kuchokera kwa Ambuye wanu motero perekani muyeso woyenera ndipo yesani zonse moyenera ndipo musachite chinyengo kwa anthu pa katundu wawo ndipo musawononge dziko lapansi pambuyo poti layeretsedwa kale. Chimenecho ndicho chinthu chabwino kwa inu ngati inu ndinu okhulupirira kwenikweni.”

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإلى مدين أخاهم شعيبا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله, باللغة نيانجا

﴿وإلى مدين أخاهم شعيبا قال ياقوم اعبدوا الله ما لكم من إله﴾ [الأعرَاف: 85]

Khaled Ibrahim Betala
“Nakonso kwa anthu aku Madiyan, (tidamtumiza) m’bale wawo Shuaib. Adati: “E inu anthu Anga! Gwadirani Allah. Mulibe mulungu wina koma Iye basi. Umboni owonekera wadza kuchokera kwa Mbuye wanu. Choncho pimani miyeso (yanu ya mbale) ndi masikelo mwachilungamo. Musawachepetsere anthu zinthu zawo; ndipo musaononge pa dziko pamhuyo polikonza. Kutero ndi kwabwino kwa inu ngati muli okhulupiriradi.”
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek