×

Kodi anthu a m’mizinda amaganiza kuti adali wotetezedwa ku chilango chathu ngati 7:97 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-A‘raf ⮕ (7:97) ayat 97 in Chichewa

7:97 Surah Al-A‘raf ayat 97 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-A‘raf ayat 97 - الأعرَاف - Page - Juz 9

﴿أَفَأَمِنَ أَهۡلُ ٱلۡقُرَىٰٓ أَن يَأۡتِيَهُم بَأۡسُنَا بَيَٰتٗا وَهُمۡ نَآئِمُونَ ﴾
[الأعرَاف: 97]

Kodi anthu a m’mizinda amaganiza kuti adali wotetezedwa ku chilango chathu ngati chikanadza kwa iwo nthawi ya usiku pamene iwo adali kugona

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أفأمن أهل القرى أن يأتيهم بأسنا بياتا وهم نائمون, باللغة نيانجا

﴿أفأمن أهل القرى أن يأتيهم بأسنا بياتا وهم نائمون﴾ [الأعرَاف: 97]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi anthu a m’mizinda (iyo momwe muli anthu oipa) ali ndi chitetezo cholimba kuti chilango chathu sichingawadzere usiku iwo ali mtulo
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek