×

Kuti tikhoza kuwayesa ndi izo. Ndi aliyense amene samvera chenjezo la Ambuye 72:17 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Jinn ⮕ (72:17) ayat 17 in Chichewa

72:17 Surah Al-Jinn ayat 17 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Jinn ayat 17 - الجِن - Page - Juz 29

﴿لِّنَفۡتِنَهُمۡ فِيهِۚ وَمَن يُعۡرِضۡ عَن ذِكۡرِ رَبِّهِۦ يَسۡلُكۡهُ عَذَابٗا صَعَدٗا ﴾
[الجِن: 17]

Kuti tikhoza kuwayesa ndi izo. Ndi aliyense amene samvera chenjezo la Ambuye wake. Iye adzakonza kuti alandire chilango chowawa zedi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لنفتنهم فيه ومن يعرض عن ذكر ربه يسلكه عذابا صعدا, باللغة نيانجا

﴿لنفتنهم فيه ومن يعرض عن ذكر ربه يسلكه عذابا صعدا﴾ [الجِن: 17]

Khaled Ibrahim Betala
“Kuti tiwayese ndi zimenezo (mmene angamyamikire Allah pa mtendere Wake pa iwo). Koma amene anyozera kupembedza Mbuye wake, amlowetsa ku chilango chovuta (chimene sangathe kupirira nacho)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek