×

Pamene Mulungu ananena ndi angelo kuti: Ndithudi Ine ndili ndi inu ndipo 8:12 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:12) ayat 12 in Chichewa

8:12 Surah Al-Anfal ayat 12 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 12 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿إِذۡ يُوحِي رَبُّكَ إِلَى ٱلۡمَلَٰٓئِكَةِ أَنِّي مَعَكُمۡ فَثَبِّتُواْ ٱلَّذِينَ ءَامَنُواْۚ سَأُلۡقِي فِي قُلُوبِ ٱلَّذِينَ كَفَرُواْ ٱلرُّعۡبَ فَٱضۡرِبُواْ فَوۡقَ ٱلۡأَعۡنَاقِ وَٱضۡرِبُواْ مِنۡهُمۡ كُلَّ بَنَانٖ ﴾
[الأنفَال: 12]

Pamene Mulungu ananena ndi angelo kuti: Ndithudi Ine ndili ndi inu ndipo limbikitsani anthu amene akhulupirira. Ine ndidzakhazikitsa mantha m’mitima ya anthu osakhulupirira, motero amenyeni m’makosi mwawo ndipo konkhonthani zala zawo za kumanja ndi za kumapazi

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إذ يوحي ربك إلى الملائكة أني معكم فثبتوا الذين آمنوا سألقي في, باللغة نيانجا

﴿إذ يوحي ربك إلى الملائكة أني معكم فثبتوا الذين آمنوا سألقي في﴾ [الأنفَال: 12]

Khaled Ibrahim Betala
“(Kumbukira) pamene Mbuye wako anawauza angelo kuti: “Ine ndili pamodzi nanu (pokulimbikitsani ndi chithandizo Changa). Alimbikitseni amene akhulupirira, ndipo ndidzathira mantha mmitima mwa amene sadakhulupirire. Choncho amenyeni mmwamba mwa makosi awo, ndi kuwadula nsonga za zala zawo (zimene akugwilira zida)
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek