×

Ngati inu mufunsa chiweruzo, tsopano chiweruzo chadza kwa inu ndipo ngati inu 8:19 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:19) ayat 19 in Chichewa

8:19 Surah Al-Anfal ayat 19 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 19 - الأنفَال - Page - Juz 9

﴿إِن تَسۡتَفۡتِحُواْ فَقَدۡ جَآءَكُمُ ٱلۡفَتۡحُۖ وَإِن تَنتَهُواْ فَهُوَ خَيۡرٞ لَّكُمۡۖ وَإِن تَعُودُواْ نَعُدۡ وَلَن تُغۡنِيَ عَنكُمۡ فِئَتُكُمۡ شَيۡـٔٗا وَلَوۡ كَثُرَتۡ وَأَنَّ ٱللَّهَ مَعَ ٱلۡمُؤۡمِنِينَ ﴾
[الأنفَال: 19]

Ngati inu mufunsa chiweruzo, tsopano chiweruzo chadza kwa inu ndipo ngati inu musiya kuchita zoipa zidzakhala bwino kwa inu ndipo ngati inu mubwerera, Ifenso tidzabwerera ndipo magulu anu a nkhondo, ngakhale kuti ndi ochuluka, sadzakuthandizani china chilichonse ndipo, ndithudi, Mulungu ali kumbali ya anthu okhulupirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: إن تستفتحوا فقد جاءكم الفتح وإن تنتهوا فهو خير لكم وإن تعودوا, باللغة نيانجا

﴿إن تستفتحوا فقد جاءكم الفتح وإن تنتهوا فهو خير لكم وإن تعودوا﴾ [الأنفَال: 19]

Khaled Ibrahim Betala
“Ngati mwakhala mukufuna chiweruzo (pogwilira nsalu yovindikira Ka’aba kuti mupambane pa nkhondo), chiweruzo chakudzerani (chokomera Asilamu). Ndipo ngati musiya (kuwazunza okhulupirira kapena kusiya kunyoza Allah) chikhala chinthu chabwino kwa inu. Koma ngati mubwereza (kuwaputa) nafenso tidzabwereza (kukulangani). Gulu lanu lankhondo silikuthandizani kanthu ngakhale lichuluke chotani. Ndipo Allah ali pamodzi ndi okhulupirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek