×

Ndipamenemudakumananawo,Mulunguadakuonetsani ngati ochepa m’maso mwanu ndipo anakuonetsani iwo inu ngati ochepa m’maso 8:44 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:44) ayat 44 in Chichewa

8:44 Surah Al-Anfal ayat 44 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 44 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿وَإِذۡ يُرِيكُمُوهُمۡ إِذِ ٱلۡتَقَيۡتُمۡ فِيٓ أَعۡيُنِكُمۡ قَلِيلٗا وَيُقَلِّلُكُمۡ فِيٓ أَعۡيُنِهِمۡ لِيَقۡضِيَ ٱللَّهُ أَمۡرٗا كَانَ مَفۡعُولٗاۗ وَإِلَى ٱللَّهِ تُرۡجَعُ ٱلۡأُمُورُ ﴾
[الأنفَال: 44]

Ndipamenemudakumananawo,Mulunguadakuonetsani ngati ochepa m’maso mwanu ndipo anakuonetsani iwo inu ngati ochepa m’maso mwawo kuti Mulungu akwaniritse lamulo lake, limene anakhazikitsa kale, ndipo ndi kwa Mulungu kumene zinthu zonse zimabwerera

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإذ يريكموهم إذ التقيتم في أعينكم قليلا ويقللكم في أعينهم ليقضي الله, باللغة نيانجا

﴿وإذ يريكموهم إذ التقيتم في أعينكم قليلا ويقللكم في أعينهم ليقضي الله﴾ [الأنفَال: 44]

Khaled Ibrahim Betala
“Ndipo (kumbukirani) pamene anakuonetsani iwo m’maso mwanu, pamene munakumana nawo kuti iwo ndi ochepa, (owerengeka, kuti mukhale ndi chidwi chomenyana nawo), ndiponso anakuchepetsani kwambiri m’maso mwawo (kuti iwo aone kuti nkosafunika kukonzekera kwambiri chifukwa chakuchepa kwa omenyana nawowo), kuti Allah akwaniritse chimene adalamula kuchitika. Kwa Allah Yekha ndiko kobwerera zinthu zonse
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek