×

oh inu anthu okhulupirira! Ngati mukumana ndi gulu la nkhondo limbikani ndipo 8:45 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:45) ayat 45 in Chichewa

8:45 Surah Al-Anfal ayat 45 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 45 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿يَٰٓأَيُّهَا ٱلَّذِينَ ءَامَنُوٓاْ إِذَا لَقِيتُمۡ فِئَةٗ فَٱثۡبُتُواْ وَٱذۡكُرُواْ ٱللَّهَ كَثِيرٗا لَّعَلَّكُمۡ تُفۡلِحُونَ ﴾
[الأنفَال: 45]

oh inu anthu okhulupirira! Ngati mukumana ndi gulu la nkhondo limbikani ndipo kumbukirani dzina la Mulungu kwambiri kuti mupambane

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ياأيها الذين آمنوا إذا لقيتم فئة فاثبتوا واذكروا الله كثيرا لعلكم تفلحون, باللغة نيانجا

﴿ياأيها الذين آمنوا إذا لقيتم فئة فاثبتوا واذكروا الله كثيرا لعلكم تفلحون﴾ [الأنفَال: 45]

Khaled Ibrahim Betala
“E inu amene mwakhulupirira! Pamene mukumana ndi gulu (la osakhulupirira) mulimbe mtima, ndipo tamandani Allah kwambiri kuti mupambane
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek