×

Mulungu tsopano wachepetsa vuto lanu chifukwa Iye adziwa kuti pakati panu pali 8:66 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:66) ayat 66 in Chichewa

8:66 Surah Al-Anfal ayat 66 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 66 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿ٱلۡـَٰٔنَ خَفَّفَ ٱللَّهُ عَنكُمۡ وَعَلِمَ أَنَّ فِيكُمۡ ضَعۡفٗاۚ فَإِن يَكُن مِّنكُم مِّاْئَةٞ صَابِرَةٞ يَغۡلِبُواْ مِاْئَتَيۡنِۚ وَإِن يَكُن مِّنكُمۡ أَلۡفٞ يَغۡلِبُوٓاْ أَلۡفَيۡنِ بِإِذۡنِ ٱللَّهِۗ وَٱللَّهُ مَعَ ٱلصَّٰبِرِينَ ﴾
[الأنفَال: 66]

Mulungu tsopano wachepetsa vuto lanu chifukwa Iye adziwa kuti pakati panu pali anthu ofoka. Motero ngati pali anthu zana limodzi opilira pakati panu iwo adzagonjetsa anthu mazana awiri, ndipo ngati pali anthu chikwi chimodzi, iwo adzagonjetsa anthu zikwi ziwiri mwachifuniro cha Mulungu. Ndipo Mulungu ali pamodzi ndi anthu opirira

❮ Previous Next ❯

ترجمة: الآن خفف الله عنكم وعلم أن فيكم ضعفا فإن يكن منكم مائة, باللغة نيانجا

﴿الآن خفف الله عنكم وعلم أن فيكم ضعفا فإن يكن منكم مائة﴾ [الأنفَال: 66]

Khaled Ibrahim Betala
“Tsopano Allah wakupeputsirani (lamulo lovutali), ndipo wadziwa kuti muli kufooka mwa inu. Choncho ngati mwa inu muli anthu zana limodzi olimba mtima adzagonjetsa mazana awiri. Ngati alipo mwa inu chikwi chimodzi, adzagonjetsa zikwi ziwiri, mwachilolezo cha Allah. Allah ali pamodzi ndi opirira
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek