×

Sikoyenera kuti Mtumwi akhale ndi akapolo a nkhondo mpaka iye atamenya nkhondo 8:67 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:67) ayat 67 in Chichewa

8:67 Surah Al-Anfal ayat 67 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 67 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿مَا كَانَ لِنَبِيٍّ أَن يَكُونَ لَهُۥٓ أَسۡرَىٰ حَتَّىٰ يُثۡخِنَ فِي ٱلۡأَرۡضِۚ تُرِيدُونَ عَرَضَ ٱلدُّنۡيَا وَٱللَّهُ يُرِيدُ ٱلۡأٓخِرَةَۗ وَٱللَّهُ عَزِيزٌ حَكِيمٞ ﴾
[الأنفَال: 67]

Sikoyenera kuti Mtumwi akhale ndi akapolo a nkhondo mpaka iye atamenya nkhondo ndi kupambana m’dziko. Inu mufuna kupeza zinthu zabwino za m’dziko lino koma Mulungu akukufunirani za m’dziko limene lili nkudza. Mulungu ndi wamphamvu ndi wanzeru

❮ Previous Next ❯

ترجمة: ما كان لنبي أن يكون له أسرى حتى يثخن في الأرض تريدون, باللغة نيانجا

﴿ما كان لنبي أن يكون له أسرى حتى يثخن في الأرض تريدون﴾ [الأنفَال: 67]

Khaled Ibrahim Betala
“Sichoyenera kwa Mneneri kukhala ndi akayidi mpaka amenye nkhondo (kwambiri) ndi kugonjetseratu maiko molimba (ndi pamene atha kukhala ndi akayidi). Mukufuna zinthu za m’dziko pomwe Allah akufuna (mupeze mphoto ya) tsiku lachimaliziro! Ndipo Allah Ngwamphamvu zoposa Ngwanzeru zakuya
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek