×

Koma ngati iwo afuna kukunyenga iwe, iwo adamunyenga kale Mulungu. Motero wakupatsa 8:71 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah Al-Anfal ⮕ (8:71) ayat 71 in Chichewa

8:71 Surah Al-Anfal ayat 71 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah Al-Anfal ayat 71 - الأنفَال - Page - Juz 10

﴿وَإِن يُرِيدُواْ خِيَانَتَكَ فَقَدۡ خَانُواْ ٱللَّهَ مِن قَبۡلُ فَأَمۡكَنَ مِنۡهُمۡۗ وَٱللَّهُ عَلِيمٌ حَكِيمٌ ﴾
[الأنفَال: 71]

Koma ngati iwo afuna kukunyenga iwe, iwo adamunyenga kale Mulungu. Motero wakupatsa iwe mphamvu kuti uwapambane iwo. Ndipo Mulungu ndi wodziwa ndi waluntha

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وإن يريدوا خيانتك فقد خانوا الله من قبل فأمكن منهم والله عليم, باللغة نيانجا

﴿وإن يريدوا خيانتك فقد خانوا الله من قبل فأمكن منهم والله عليم﴾ [الأنفَال: 71]

Khaled Ibrahim Betala
“Ngati akufuna kukuchitirani chinyengo (chinyengo chawo sichiphula kanthu pa iwe), ndithu anamuchitirapo kale Allah chinyengo (chifukwa cha kusakhulupirira kwawo). Choncho anakupatsa mphamvu zowagonjetsera iwo. Ndipo Allah Ngodziwa, Ngwanzeru zakuya
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek