×

Ndipo pakati pa Maarabu amene amakhala m’chipululu amene akuzungulira iwe, ena ndi 9:101 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:101) ayat 101 in Chichewa

9:101 Surah At-Taubah ayat 101 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 101 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿وَمِمَّنۡ حَوۡلَكُم مِّنَ ٱلۡأَعۡرَابِ مُنَٰفِقُونَۖ وَمِنۡ أَهۡلِ ٱلۡمَدِينَةِ مَرَدُواْ عَلَى ٱلنِّفَاقِ لَا تَعۡلَمُهُمۡۖ نَحۡنُ نَعۡلَمُهُمۡۚ سَنُعَذِّبُهُم مَّرَّتَيۡنِ ثُمَّ يُرَدُّونَ إِلَىٰ عَذَابٍ عَظِيمٖ ﴾
[التوبَة: 101]

Ndipo pakati pa Maarabu amene amakhala m’chipululu amene akuzungulira iwe, ena ndi anthu a chinyengo, chimodzi modzi anthu ena a ku Medina. Iwo amanena zabodza ndipo ndi a chinyengo. Iwe siuwadziwa koma Ife timawadziwa. Ife tidzawalanga kawiri ndipo pambuyo pake adzabwezedwa ku chilango chachikulu

❮ Previous Next ❯

ترجمة: وممن حولكم من الأعراب منافقون ومن أهل المدينة مردوا على النفاق لا, باللغة نيانجا

﴿وممن حولكم من الأعراب منافقون ومن أهل المدينة مردوا على النفاق لا﴾ [التوبَة: 101]

❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek