×

Usapemphere m’menemu. Ndithudi Mzikiti umene udamangidwa ndi cholinga chomuopa Mulungu kuchokera tsiku 9:108 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:108) ayat 108 in Chichewa

9:108 Surah At-Taubah ayat 108 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 108 - التوبَة - Page - Juz 11

﴿لَا تَقُمۡ فِيهِ أَبَدٗاۚ لَّمَسۡجِدٌ أُسِّسَ عَلَى ٱلتَّقۡوَىٰ مِنۡ أَوَّلِ يَوۡمٍ أَحَقُّ أَن تَقُومَ فِيهِۚ فِيهِ رِجَالٞ يُحِبُّونَ أَن يَتَطَهَّرُواْۚ وَٱللَّهُ يُحِبُّ ٱلۡمُطَّهِّرِينَ ﴾
[التوبَة: 108]

Usapemphere m’menemu. Ndithudi Mzikiti umene udamangidwa ndi cholinga chomuopa Mulungu kuchokera tsiku loyamba ndi woyenera kuti iwe upemphere mmenemo. Mmenemo muli anthu okonda kudziyeretsa. Ndipo Mulungu amakonda iwo amene amadziyeretsa

❮ Previous Next ❯

ترجمة: لا تقم فيه أبدا لمسجد أسس على التقوى من أول يوم أحق, باللغة نيانجا

﴿لا تقم فيه أبدا لمسجد أسس على التقوى من أول يوم أحق﴾ [التوبَة: 108]

Khaled Ibrahim Betala
“Usaimilire (ndi kupemphera) m’menemo mpang’ono pomwe. Ndithu msikiti umene udakhazikitsidwa poyamba ncholinga choopa Allah ndiwo wofunika kuti uimilire m’menemo (ndi kupemphera). M’menemo muli anthu okonda kudziyeretsa (matupi ndi mitima yawo); ndipo Allah amakonda odziyeretsa
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek