×

Kodi inu mukuganiza kuti mudzasiyidwa nokhanokha pamene Mulungu sadawayese iwo amene ali 9:16 Chichewa translation

Quran infoChichewaSurah At-Taubah ⮕ (9:16) ayat 16 in Chichewa

9:16 Surah At-Taubah ayat 16 in Chichewa (نيانجا)

Quran with Chichewa translation - Surah At-Taubah ayat 16 - التوبَة - Page - Juz 10

﴿أَمۡ حَسِبۡتُمۡ أَن تُتۡرَكُواْ وَلَمَّا يَعۡلَمِ ٱللَّهُ ٱلَّذِينَ جَٰهَدُواْ مِنكُمۡ وَلَمۡ يَتَّخِذُواْ مِن دُونِ ٱللَّهِ وَلَا رَسُولِهِۦ وَلَا ٱلۡمُؤۡمِنِينَ وَلِيجَةٗۚ وَٱللَّهُ خَبِيرُۢ بِمَا تَعۡمَلُونَ ﴾
[التوبَة: 16]

Kodi inu mukuganiza kuti mudzasiyidwa nokhanokha pamene Mulungu sadawayese iwo amene ali pakati panu, amene adamenya nawo nkhondo mwachamuna ndipo sadachite ubwenzi ndi wina kupatula Mulungu ndi Mtumwi wake ndi anthu okhulupirira? Mulungu amadziwa zimene mumachita

❮ Previous Next ❯

ترجمة: أم حسبتم أن تتركوا ولما يعلم الله الذين جاهدوا منكم ولم يتخذوا, باللغة نيانجا

﴿أم حسبتم أن تتركوا ولما يعلم الله الذين جاهدوا منكم ولم يتخذوا﴾ [التوبَة: 16]

Khaled Ibrahim Betala
“Kodi mukuganiza kuti mungosiidwa chabe Allah asanawaonetsere poyera amene amenyera chipembedzo mwa inu ndi amene sachita ubwenzi (ndi wina wake) kupatula Allah ndi Mtumiki wake ndi okhulupirira? Ndipo Allah Ngodziwa zonse zimene muchita
❮ Previous Next ❯

Verse in more languages

Transliteration Bangla Bosnian German English Persian French Hindi Indonesian Kazakh Dutch Russian Spanish Turkish Urdu Uzbek